Jeremiah 46:23 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adzaduladi nkhalango ya ku Ejipito ngakhale njoŵirira, chifukwa anthuwo ndi ochuluka ngati dzombe, sangathe kuŵerengeka.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Adzatema nkhalango yake, ati Yehova, pokhala yosapitika; pakuti achuluka koposa dzombe, ali osawerengeka.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iwo adzadula nkhalango ya Igupto,” akutero Yehova, “ngakhale kuti ndi yowirira. Anthuwo ndi ochuluka kupambana dzombe, moti sangatheke kuwerengeka.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Adzatema nkhalango yace, ati Yehova, pokhala yosapitika; pakuti acuruka koposa dzombe, ali osawerengeka.