Jeremiah 46:24 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu a ku Ejipito adzachitadi manyazi, adzatengedwa ukapolo ndi anthu akumpoto,” akutero Chauta.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mwana wake wamkazi wa Ejipito adzachitidwa manyazi, adzaperekedwa m'manja a anthu a kumpoto.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anthu a ku Igupto achita manyazi atengedwa ukapolo ndi anthu a kumpoto.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mwana wace wamkazi wa Aigupto adzacitidwa manyazi, adzaperekedwa m'manja a anthu a kumpoto.