Jeremiah 46:3 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Konzani zishango ndi malihawo, yambanipo wa ku nkhondo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Konzani chikopa ndi lihawo, nimuyandikire kunkhondo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
anati, “Konzani zishango zanu ndi malihawo, ndipo yambanipo kupita ku nkhondo!
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Konzani cikopa ndi lihawo, nimuyandikire kunkhondo.