Jeremiah 46:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Waliŵiro sangathe kupulumuka. Ngakhale wankhondo wamphamvu sangathe kudzipulumutsa. Akunka naphunthwa, kumagwa kumpoto kwa mtsinje wa Yufurate.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Waliwiro asathawe, wamphamvu asapulumuke; kumpoto pambali pa mtsinje wa Yufurate waphunthwa nagwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Waliwiro sangathe kuthawa ngakhale wankhondo wamphamvu sangathe kupulumuka. Akunka napunthwa ndi kugwa kumpoto kwa mtsinje wa Yufurate.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Waliwiro asathawe, wamphamvu asapulumuke; kumpoto pambali pa nyanja ya Firate wapunthwa nagwa.