Jeremiah 46:7 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Kodi ndani akukwera ngati mtsinje wa Nailo, ngati mitsinje ya madzi achigumula?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndani uyu amene auka ngati Nailo, madzi ake ogavira monga nyanja?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Kodi ndani amene akukwera ngati Nailo, ngati mtsinje wa madzi amkokomo?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndani uyu amene auka ngati Nile, madzi ace ogabvira monga nyanja?