Jeremiah 48:14 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Kodi mungathe kunena bwanji kuti, ‘Ife ndife ngwazi, asilikali olimba mtima pa nkhondo?’
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Muti bwanji, Tili amphamvu, olimba mtima ankhondo?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Kodi munganene bwanji kuti, ‘Ife ndife asilikali. Ife ndife ngwazi, anthu amphamvu pa nkhondo?’
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Muti bwanji, Tiri amphamvu, olimba mtima ankhondo?