Jeremiah 48:5 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu akupita nalira kwambiri pa chikwera cha ku Luhiti. Kulira kwa chiwonongeko kukumveka ku matsitso a ku Horonaimu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti adzakwera pa chikweza cha Luhiti ndi kulira kosaleka; pakuti pa chitsiko cha Horonaimu amva kulira kowawa kwa chionongeko.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anthu akukwera chikweza cha ku Luhiti, akulira kwambiri pamene akupita. Kulira chifukwa cha chiwonongeko kukumveka pa njira yotsikira ku Horonaimu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti adzakwera pa cikweza ca Luhiti ndi kulira kosaleka; pakuti pa citsiko ca Horonaimu amva kulira kowawa kwa cionongeko.