Jeremiah 5:18 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Koma ngakhale pa masiku amenewo sindidzakuwonongani kotheratu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma masiku onsewo, ati Yehova, sindidzatsirizitsa konse ndi iwe.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Komabe pa masiku amenewo sindidzakuwonongani kotheratu,” akutero Yehova.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma masiku onsewo, ati Yehova, sindidzatsirizitsa konse ndi iwe.