Jeremiah 5:21 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Imvani izi, inu anthu opusa, opanda ndi nzeru zomwe, inu amene maso muli nawo, koma simupenya, amene makutu muli nawo, koma simumva.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Tamvanitu ichi, inu anthu opusa, ndi opanda nzeru; ali ndi maso koma osaona, ali ndi makutu koma osamva;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Imvani izi, inu anthu opusa ndi opanda nzeru, inu amene maso muli nawo koma simupenya, amene makutu muli nawo koma simumva.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Tamvanitu ici, inu anthu opusa, ndi opanda nzeru; ali ndi maso koma osaona, ali ndi makutu koma osamva;