Jeremiah 5:30 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
M'dziko muno mwachitika chinthu chododometsa ndi choopsa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chodabwitsa ndi choopsa chaoneka m'dzikomo;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Chinthu chothetsa nzeru ndi choopsa kwambiri chachitika mʼdzikomo:
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Codabwitsa ndi coopsya caoneka m'dzikomo;