Jeremiah 50:31 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Ndikukuthira nkhondo, mzinda wachipongwewe, pakuti yakwana nthaŵi yako, lafika tsiku lako la chilango,” akutero Chauta Wamphamvuzonse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Taonani, nditsutsana nawe, wonyada iwe, ati Ambuye, Yehova wa makamu; pakuti tsiku lako lafika, nthawi imene ndidzakulanga iwe.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Taona, ndikukuthira nkhondo, iwe wodzikuzawe,” akutero Ambuye Yehova Wamphamvuzonse, “chifukwa tsiku lako lafika, nthawi yoti ndikulange yakwana.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Taonani, nditsutsana nawe, wonyada iwe, ati Ambuye, Yehova wa makamu; pakuti tsiku lako lafika, nthawi imene ndidzakulanga iwe.