Jeremiah 6:12 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nyumba zao zidzapatsidwa kwa ena pamodzi ndi minda yao ndi akazi ao omwe. Ndithuditu, ndi dzanja langali ndidzakantha anthu okhala m'dzikomo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Nyumba zao zidzasanduka za ena, pamodzi ndi minda yao ndi akazi ao; pakuti ndidzatambasula dzanja langa pa okhala m'dziko, ati Yehova.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nyumba zawo adzazipereka kwa ena, pamodzi ndi minda yawo ndi akazi awo. Ndidzatambasula dzanja langa kukantha anthu okhala mʼdzikomo,” akutero Yehova.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Nyumba zao zidzasanduka za ena, pamodzi ndi minda yao ndi akazi ao; pakuti ndidzatambasula dzanja langa pa okhala m'dziko, ati Yehova.