Jeremiah 6:17 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chauta adakupatsani alonda oti akutsogolereni nati, ‘Imvani kulira kwa lipenga lokuchenjezani.’ Koma inu mudati, ‘Sitidzasamalako.’
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo ndinaika alonda oyang'anira inu, ndi kuti, Mverani mau a lipenga; koma anati, Sitidzamvera.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ine ndinakupatsani alonda oti akuyangʼanireni ndipo ndinati, ‘Imvani kulira kwa lipenga!’ koma inu munati, ‘Sitidzamvera.’
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo ndinaika alonda oyang'anira inu, ndi kuti, Mverani mau a lipenga; koma anati, Sitidzamvera.