Jeremiah 6:27 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Iwe Yeremiya, ndakusankha kuti ukhale choyesera zitsulo. Uŵayese anthu anga kuti uwone m'mene aliri makhalidwe ao.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndakuyesa iwe nsanja ndi linga mwa anthu anga, kuti udziwe ndi kuyesa njira yao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Iwe Yeremiya, ndakuyika kuti ukhale choyesera zitsulo. Uwayese anthu anga monga ungayesere chitsulo kuti uwone makhalidwe awo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndakuyesa iwe nsanja ndi linga mwa anthu anga, kuti udziwe ndi kuyesa njira yao.