Jeremiah 7:8 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Koma onani, inu mumakhulupirira mabodza.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Taonani, mukhulupirira mau onama, osapindulitsa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma onani, inu mukudalira mawu abodza amene alibe phindu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Taonani, mukhulupirira mau onama, osapindulitsa.