Jeremiah 8:15 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tinkafuna mtendere, koma zinthu sizidatiyendere bwino. Tinkafuna kuchira, koma tidangopeza zoopsa zokhazokha.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Tinayang'anira mtendere, koma panalibe zabwino; ndi nthawi ya moyo, ndipo taona kuopsedwa!
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tinkayembekezera mtendere koma palibe chabwino chomwe chinachitika, tinkayembekezera kuchira koma tinakumana ndi zoopsa zokhazokha.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Tinayang'anira mtendere, koma panalibe zabwino; ndi nthawi ya moyo, ndipo taona kuopsedwa!