Jeremiah 8:20 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu akuti, “Kholola lapita, chilimwe chapita, koma sitidapulumukebe.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Masika apita, mphakasa yatha, ndipo ife sitinapulumutsidwe.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Nthawi yokolola yapita, chilimwe chapita, koma sitinapulumuke.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Masika apita, mphakasa yatha, ndipo ife sitinapulumutsidwe.