Jeremiah 8:21 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndikumva kuŵaŵa chifukwa cha mavuto a anthu anga, ndikungolira, nkhaŵa yandigwira.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Bala la mwana wamkazi wa anthu anga ndaphwetekwa nalo; ndada mtima; kudabwa kwandigwira.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Chifukwa cha mavuto a anthu anga, ine ndikumva kuwawa; ndikungolira ndipo mantha aakulu andigwira.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Bala la mwana wamkazi wa anthu anga ndaphwetekwa nalo; ndada mtima; kudabwa kwandigwira.