Jeremiah 9:1 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndikadakonda kuti mutu wanga ukhale ngati chitsime cha madzi, kuti maso anga akhale ngati kasupe wa misozi, kuti ndilire usana ndi usiku, kulirira onse amene adafa a mtundu wa anthu anga?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ha, mutu wanga ukadakhala madzi, ndi maso anga kasupe wa misozi, kuti usana ndi usiku ndilirire ophedwa a mwana wamkazi wa anthu anga!
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Aa, ndikanakonda kuti mutu wanga ukanakhala chitsime cha madzi, ndi maso anga ngati kasupe wa misozi! Ndikanalira usana ndi usiku kulirira anthu anga amene aphedwa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ha, mutu wanga ukadakhala madzi, ndi maso anga kasupe wa misozi, kuti usana ndi usiku ndilirire ophedwa a mwana wamkazi wa anthu anga!