Jeremiah 9:14 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma ankangotsata zolakwa za mitima yao yokanika. Ankapembedza Abaala monga momwe makolo ao adaŵaphunzitsira.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
koma anatsata kuuma kwa mtima wao, ndi Baala, monga makolo ao anawaphunzitsa;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mʼmalo mwake, anatsatira zolakwa za mʼmitima yawo; anapembedza Abaala ngati momwe makolo awo anawaphunzitsira.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
koma anatsata kuuma kwa mtima wao, ndi Baala, monga makolo ao anawaphunzitsa;