Jeremiah 9:18 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu akuti, “Abwere mofulumira adzatilire kuti m'maso mwathu mudze misozi nsidze zathu zinyowe.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
afulumire, atikwezere ife mau a maliro, kuti maso athu agwe misozi, ndi zikope zathu ziyendetse madzi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anthu akuti, “Abwere mofulumira kuti adzatilire mpaka mʼmaso mwathu mutatuluka misozi ndi kuti msidze zathu zinyowe ndi madzi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
afulumire, atikwezere ife mau a maliro, kuti maso athu agwe misozi, ndi zikope zathu ziyendetse madzi.