Jeremiah 9:25 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chauta akunena kuti, “Nthaŵi ikubwera pamene ndidzalanga onse oumbalidwa, amene mu mtima sasamalako.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Taonani, masiku alikudza, ati Yehova, kuti ndidzalanga onse odulidwa m'kusadulidwa kwao;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Nthawi ikubwera,” akutero Yehova, “pamene ndidzalanga onse amene anachita mdulidwe koma mu mtima sasamala nʼkomwe.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Taonani, masiku alikudza, ati Yehova, kuti ndidzalanga onse odulidwa m'kusadulidwa kwao;