Jeremiah 9:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Amasanjikiza tchimo pa tchimo linzake, chinyengo pa chinyengo chinzake. Amakana kundidziŵa,” akuterotu Chauta.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ukhala pakati pa manyengo m'manyengo; akana kundidziwa, ati Yehova.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iwe wakhalira mʼchinyengo ndipo ukukana kundidziwa Ine,” akutero Yehova.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ukhala pakati pa manyengo m'manyengo; akana kundidziwa, ati Yehova.