Job 1:15 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mwadzidzidzi nkubwera Aseba kudzatithira nkhondo nalanda ng'ombezo ndi abulu omwe. Ndipo apha antchito onse, koma ine ndekha ndiye ndapulumuka kuti ndidzakuuzeni.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
koma anazigwera Aseba, nazitenga, nawapha anyamata ndi lupanga lakuthwa, ndipo ndapulumuka ine ndekha kudzakuuzani.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
tsono panabwera Aseba kudzatithira nkhondo ndi kutenga zonse. Apha antchito ndi lupanga, ndipo ine ndekha ndiye ndapulumuka kuti ndidzakuwuzeni!”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
koma anazigwera Aseba, nazitenga, nawapha anyamata ndi lupanga lakuthwa, ndipo ndapulumuka ine ndekha kudzakuuzani.