Job 1:2 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anali ndi ana aamuna asanu ndi aŵiri, ndi ana aakazi atatu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anabala ana amuna asanu ndi awiri, ndi ana akazi atatu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anali ndi ana aamuna asanu ndi awiri ndi ana aakazi atatu,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anabala ana amuna asanu ndi awiri, ndi ana akazi atatu.