Job 11:12 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Paja amati, Chitsiru nchitsiru ndithu, ndipo nyama ndi nyama ndithu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma munthu wopanda pake asowa nzeru, ngakhale munthu abadwa ngati mwanawabulu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu wopanda nzeru sizingatheke kukhala wanzeru monganso mwana wa bulu wakuthengo sangasanduke munthu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma munthu wopanda pace asowa nzeru, Ngakhale munthu abadwa ngati mwana wa mbidzi.