Job 11:16 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Zoŵaŵa zakozi udzaziiŵala, zidzakhala ngati madzi amene apita kale.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
pakuti udzaiwala chisoni chako, udzachikumbukira ngati madzi opita.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Udzayiwala ndithu zowawa zako, zidzakhala ngati madzi amene apita kale.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti udzaiwala cisoni cako, Udzacikumbukila ngati madzi opita;