Job 14:1 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Munthu wobadwa mwa mkazi amakhala masiku oŵerengeka, komanso masiku ake ndi amavuto okhaokha.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Munthu wobadwa ndi mkazi ngwa masiku owerengeka, nakhuta mavuto.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Munthu wobadwa mwa amayi amakhala masiku owerengeka ndipo ndi odzaza ndi mavuto okhaokha.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Munthu wobadwa ndi mkazi Ngwa masiku owerengeka, nakhuta mabvuto,