Job 14:10 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma munthu akafa, kutha kwake nkomweko. Kodi munthuyo akafa, amapita kuti?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma munthu akufa atachita liondeonde inde, munthu apereka mzimu wake, ndipo ali kuti?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma munthu amafa nayikidwa mʼmanda, amapuma mpweya wotsiriza ndipo kutha kwake nʼkomweko.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma munthu akufa atacita liondeonde Inde, munthu apereka mzimu wace, ndipo ali kuti?