Job 14:11 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Monga madzi amaphwa m'nyanja, monganso mtsinje umaphwa nuuma,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Madzi achoka m'nyanja, ndi mtsinje ukuphwa, nuuma;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Monga madzi amaphwera mʼnyanja kapena monga mtsinje umaphwera nuwuma,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Madzi acoka m'nyanja, Ndi mtsinje ukuphwa, nuuma;