Job 14:22 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Amangomva zoŵaŵa za m'thupi mwake zokha, amangodzilira yekha mwiniwakeyo.” Elifazi
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma thupi lake limuwawira yekha, ndi mtima wake umliritsa yekha.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye amangomva zowawa za mʼthupi lake ndipo amangodzilirira yekha mwini wakeyo.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma thupi lace limuwawira yekha, Ndi mtima wace umliritsa yekha.