Job 14:9 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
komabe chinyontho chikafika, udzaphukira, udzaphukadi nthambi ngati mtengo wanthete.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma pa mnunkho wa madzi udzaphuka, nudzaswa nthambi ngati womera.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
koma pamene chinyontho chafika udzaphukira ndipo udzaphuka nthambi ngati mtengo wanthete.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma pa mnunkho wa madzi udzaphuka, Nudzaswa nthambi ngati womera.