Job 15:11 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kodi akukuchepera mau othuzitsa mtima ochokera kwa Mulunguŵa, kapena mau okulankhula mofatsaŵa?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Masangalatso a Mulungu akuchepera kodi? Kapena uli nacho chinsinsi kodi?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kodi mawu otonthoza mtima ochokera kwa Mulungu sakukukwanira, mawu oyankhula mofatsawa kwa iwe?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Masangalatso a Mulungu akucepera kodi? Kapena uli naco cinsinsi kodi?