Job 15:14 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kodi munthu nchiyani kuti angathe kukhala wosachimwa? Kapena wobadwa kwa mkazi nchiyani, kuti angakhale wopanda uchimo pamaso pa Mulungu?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Munthu nchiyani kuti akhale woyera, wobadwa ndi mkazi kuti akhale wolungama?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Kodi munthu nʼchiyani kuti nʼkukhala woyera mtima kapena wobadwa mwa amayi nʼchiyani kuti nʼkukhala wolungama mtima?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Munthu nciani kuti akhale woyera, Wobadwa ndi mkazi kuti akhale wolungama?