Job 15:16 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nanji tsono munthu, amene ali wonyansa ndi wachabechabe, amene kuchita zoipa kuli ngati kumwa madzi!
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koposa kotani nanga munthu wonyansa ndi wodetsa, wakumwa chosalungama ngati madzi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
nanga kuli bwanji munthu amene ndi wonyansa ndi wa njira zokhotakhota, amene kuchita zoyipa kuli ngati kumwa madzi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koposa kotani nanga munthu wonyansa ndi wodetsa, Wakumwa cosalungama ngati madzi.