Job 15:18 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Zoonazo adandiphunzitsa ndi anthu anzeru, sadandibisire zimene adamva kwa makolo ao.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
chimene adachinena anzeru, adachilandira kwa makolo ao, osachibisa;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
zimene anandiphunzitsa anthu anzeru, sanandibisire kalikonse kamene anamva kuchokera kwa makolo awo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cimene adacinena anzeru, Adacilandira kwa makolo ao, osacibisa;