Job 15:19 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Dziko lao linali lopanda anthu achilendo, amene adakaŵachotsa mu njira yake ya Mulungu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndiwo amene analandira okha dzikoli, wosapita mlendo pakati pao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
(Ndi kwa iwowa kumene dziko lino linaperekedwa pamene panalibe mlendo wokhala pakati pawo).
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndiwo amene analandira okha dzikoli, Wosapita mlendo pakati pao;