Job 15:21 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Amamva mau oopsa m'makutu mwake, pamene akuyesa kuti ali pabwino, achifwamba adzamthira nkhondo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
M'makutu mwake mumveka zoopsetsa; pali mtendere amfikira wakumuononga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Amamva mawu owopsa mʼmakutu mwake, pamene zonse zikuoneka ngati zili bwino, anthu achifwamba amamuthira nkhondo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
M'makutu mwace mumveka zoopsetsa; Pali mtendere amfikira wakumuononga.