Job 15:22 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Sakhulupirira kuti angathe kupulumuka ku mdima wa imfa, akuyenera kuphedwa ndithu basi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Sakhulupirira kuti adzatulukamo mumdima, koma kuti lupanga limlindira.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye sakhulupirira kuti angathe kupulumuka ku mdima wa imfa; iyeyo ndi woyenera kuphedwa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Sakhulupirira kuti adzaturukamo mumdima, Koma kuti lupanga limlindira;