Job 15:23 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Amangoyendayenda paliponse, kunka nafuna chakudya nkumati, ‘Kodi chili kuti?’ Amadziŵa kuti tsiku lamdima lili pafupi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ayendayenda ndi kufuna chakudya, nati, Chilikuti? Adziwa kuti lamkonzekeratu pafupi tsiku lamdima.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Amangoyendayenda pali ponse kunka nafuna chakudya; amadziwa kuti tsiku la mdima lili pafupi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ayendayenda ndi kufuna cakudya, nati, Ciri kuti? Adziwa kuti lamkonzekeratu pafupi tsiku lamdima,