Job 15:24 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Masautso ndi nthumanzi zimamchititsa mantha kwambiri. Zimenezi zimamgudukira koopsa, monga imachitira mfumu imene yakonzekera kukamenya nkhondo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Nsautso ndi chipsinjo zimchititsa mantha, zimlaka ngati mfumu yokonzekeratu kunkhondo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Masautso ndi nthumanzi zimamuchititsa mantha kwambiri; zimamugonjetsa iye monga imachitira mfumu yokonzekera kukathira nkhondo,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Nsautso ndi cipsinjo zimcititsa mantha, Zimlaka ngati mfumu yokonzekeratu kunkhondo;