Job 15:27 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Ngakhale nkhope yake ndi yokulupala, ngakhale m'chiwuno mwake muli monenepa kwambiri,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Popeza anakuta nkhope yake ndi kunenepa kwake, nachita mafunyenye a mafuta m'zuuno zake;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Ngakhale nkhope yake ndi yonenepa ndipo mʼchiwuno mwake muli mnofu wambiri,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Popeza anakuta nkhope yace ndi kunenepa kwace, Nacita mafunyenye a mafuta m'zuuno zace;