Job 15:28 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
munthuyo adzasauka m'mizinda yoonongeka. Adzakhala m'nyumba zosayenera kukhalamo anthu, chifukwa zidaonongeka pa nkhondo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
adzakhala m'midzi yopasuka, m'nyumba zosakhalamo munthu, zoti zisandulika muunda.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
munthuyo adzakhala mʼmizinda yowonongeka ndi mʼnyumba zosayenera kukhalamo anthu, nyumba zimene zikugwa ndi kuwonongeka.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Adzakhala m'midzi yopasuka, M'nyumba zosakhalamo munthu, Zoti zisandulika muunda.