Job 15:35 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ameneŵa ndiwo amalingalira zaupandu namachita zoipa. Mtima wao umaganizira zonyenga nthaŵi zonse.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Aima ndi chovuta, nabala mphulupulu, ndi m'mimba mwao mukonzeratu chinyengo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iwo amalingalira zaupandu ndipo amachita zoyipa; mtima wawo umakonzekera zachinyengo.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Aima ndi cobvuta, nabala mphulupulu, Ndi m'mimba mwao mukonzeratu cinyengo.