Job 15:4 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma iwe ukufuna kuti anthu asamaope Mulungu, ukufuna kuti aleke kusinkhasinkha za Mulungu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Zedi uyesa chabe mantha, nuchepsa chilingiriro pamaso pa Mulungu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma iwe ukuchepetsa zoopa Mulungu ndipo ukutchinga zodzikhuthulira kwa Mulungu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Zedi uyesa cabe mantha, Nucepsa cilingiriro pamaso pa Mulungu.