Job 16:11 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mulungu wandipereka kwa anthu osasamala za Iye, wandiponya m'manja mwa anthu oipa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mulungu andipereka kwa osulangama, nandiponya m'manja a oipa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mulungu wandipereka kwa anthu ochita zoyipa ndipo wandiponyera mʼmanja mwa anthu oyipa mtima.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mulungu andipereka kwa osalungama, Nandiponya m'manja a oipa.