Job 16:2 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Zoterezi ndidazimva kale. Nonsenu ndinu anthu osatha kuthuzitsa mtima mnzanu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndamva zambiri zotere; inu nonse ndinu otonthoza mtima mondilemetsa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Ndinamvapo zambiri monga zimenezi; nonsenu ndinu anthu osatha kutonthoza mtima mnzanu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndamva zambiri zotere; Inu nonse ndinu otonthoza mtima mondilemetsa.