Job 16:7 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndithudi, Mulungu wanditha mphamvu, waononga banja langa lonse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma tsopano wandilemetsa Iye; mwapasula msonkhano wanga wonse.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndithudi, Inu Mulungu mwanditha mphamvu; mwawononga banja langa lonse.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma tsopano wandilemetsa Iye; Mwapasula msonkhano wanga wonse.