Job 20:17 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Sadzaona mitsinje ya mafuta a olivi, kapena mifuleni ya madalitso a m'dziko lamwanaalirenji.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Sadzapenyerera timitsinje, toyenda nao uchi ndi mafuta.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Sadzasangalala ndi timitsinje, mitsinje yoyenda uchi ndi mafuta.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Sadzapenyerera timitsinje, Toyenda nao uci ndi mafuta.