Job 20:4 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kodi sukudziŵa zimene zidachitika masiku amakedzana, kuyambira nthaŵi imene munthu adalengedwa pa dziko.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kodi suchidziwa ichi chiyambire kale lomwe, nuyambira anaika munthu pa dziko lapansi,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Ndithudi iwe ukudziwa momwe zinthu zakhala zikuchitikira kuyambira kale, kuchoka nthawi imene munthu analengedwa pa dziko lapansi,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kodi sucidziwa ici ciyambire kale lomwe, Kuyambira anaika munthu pa dziko lapansi,